23 Davide nati, Simudzatero, abale anga inu, ndi zimene anatipatsa ife Yehova, amene anatisunga, napereka m'dzanja lathu khamu lija linadza kumenyana nafe.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 30
Onani 1 Samueli 30:23 nkhani