1 Samueli 31:7 BL92

7 Ndipo pamene Aisrayeli akukhala tsidya lina la cigwa, ndi iwo akukhala tsidya la Yordano, anaona kuti Aisrayeli alikuthawa, ndi kuti Sauli ndi ana ace anafa, iwowa anasiya midzi yao, nathawa; ndipo Afilisti anadza nakhala m'menemo.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 31

Onani 1 Samueli 31:7 nkhani