20 Ndipo pamene adati amwalire, anthu akazi akukhala naye ananena, Usaope, popeza waona mwana wamwamuna. Koma iye sanayankha, kapena kusamalira.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 4
Onani 1 Samueli 4:20 nkhani