1 Samueli 4:7 BL92

7 Ndipo Afilisti anaopa, pakuti anati, Mulungu wafika kuzithando. Ndipo iwo anati, Tsoka kwa ife! popeza kale lonse panalibe cinthu cotere.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 4

Onani 1 Samueli 4:7 nkhani