1 Samueli 7:14 BL92

14 Ndipo midzi ya Israyeli imene Afilisti adailanda kale inabwezedwa kwa Aisrayeli, kuyambira ku Ekroni kufikira ku Gati; ndi Aisrayeli analanditsa miraga yao m'manja a Afilisti. Ndipo pakati pa Aisrayeli ndi Aamori panali mtendere;

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 7

Onani 1 Samueli 7:14 nkhani