2 Iye anali ndi mwana wamwamuna dzina lace Sauli, mnyamata wokongola; pakati pa anthu onse a Israyeli panalibe wina wokongola ngati iye; anali wamtali, anthu onse ena anamlekeza m'cifuwa.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 9
Onani 1 Samueli 9:2 nkhani