Luka 6:9 BL92

9 Ndipo Iyeananyamuka, naimirira. Ndipo Yesuanati kwa iwo, Ndikufunsani inu, Kodi nkulola tsiku la Sabata, kucita zabwino, kapena kucita zoipa? kupulumutsa moyo, kapena kuuononga?

Werengani mutu wathunthu Luka 6

Onani Luka 6:9 nkhani