12 anauka ngwazi zonse, nacotsa mtembo wa Sauli, ndi mitembo ya ana ace, nabwera nayo ku Yabesi, naika mafupa ao patsinde pa mtengo wathundu ku Yabesi, nasala masiku asanu ndi awiri.
Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 10
Onani 1 Mbiri 10:12 nkhani