1 Mbiri 11:10 BL92

10 Akuru a amphamvu aja Davide anali nao akulimbika pamodzi naye m'ufumu wace, pamodzi ndi Aisrayeli onse, kumlonga ufumu, monga mwa mau a Yehova akunena za Israyeli, ndi awa.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 11

Onani 1 Mbiri 11:10 nkhani