1 Mbiri 13:6 BL92

6 Ndipo Davide ndi Aisrayeli onse pamodzi naye anakwera kumka ku Baala, ndiko ku Kiriati-Yearimu wa m'Yuda, kukwera nalo kucokera komweko likasa la Mulungu Yehova wakukhala pa akerubi, kumene aitanirako Dzina.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 13

Onani 1 Mbiri 13:6 nkhani