11 Atafika tsono ku Baala Perazimu, Davide anawakantha komweko; nati Davide, Mulungu anapasula adani anga ndi dzanja langa, ngati pokhamulira madzi. Cifukwa cace analicha dzina la malowo Baala Perazimu.
Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 14
Onani 1 Mbiri 14:11 nkhani