1 Mbiri 17:24 BL92

24 Inde likhazikike dzina lanu, likulitsidwe kosalekeza, ndi kuti, Yehova wa makamu ndiye Mulungu wa Israyeli; akhalira Israyeli Mulungu; ndi nyumba ya Davide mtumiki wanu ikhazikika pamaso panu.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 17

Onani 1 Mbiri 17:24 nkhani