1 Mbiri 17:6 BL92

6 Pali ponse ndinayenda nao Aisrayeli onse ndinanena kodi mau ndi woweruza ali yense wa Israyeli, amene ndinamuuza adyetse anthu anga, ndi kuti, Mwalekeranji kundimangira nyumba yamikungudza?

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 17

Onani 1 Mbiri 17:6 nkhani