1 Mbiri 19:16 BL92

16 Ndipo pakuona Aaramu kuti Israyeli anawakantha, anatumiza mithenga, naturuka nao Aaramu akukhala tsidya lija la mtsinjewo; ndi Sofaki kazembe wa khamu la Hadarezeri anawatsogolera.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 19

Onani 1 Mbiri 19:16 nkhani