1 Mbiri 19:2 BL92

2 Ndipo Davide anati, Ndidzamcitira zokoma mtima Hanuni mwana wa Nahasi, popeza atate wace anandicitira ine zokoma mtima. Momwemo Davide anatuma mithenga imtonthoze mtima pa atate wace. Pofika anyamata ace a Davide ku dziko la ana a Amoni kwa Hanuni kumtonthoza mtima,

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 19

Onani 1 Mbiri 19:2 nkhani