1 Mbiri 19:3 BL92

3 akalonga a ana a Amoni anati kwa Hanuni, Davide ali kucitira atate wanu ulemu kodi, popeza anakutumizirani otonthoza? sakudzerani kodi anyamata ace kufunafuna, ndi kugubuduza, ndi kuzonda dziko?

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 19

Onani 1 Mbiri 19:3 nkhani