5 Pamenepo anamuka ena, namuuza Davide za amunawa. Natumiza iye kukomana nao, pakuti amunawa anacita manyazi kwambiri. Ndipo mfumu inati, Balindani ku Yeriko mpaka zamera ndebvu zanu; zitamera mubwere.
Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 19
Onani 1 Mbiri 19:5 nkhani