1 Mbiri 21:16 BL92

16 Ndipo Davide anakweza maso ace, naona mthenga wa Yehova alikuima pakati pa dziko ndi thambo, ali nalo lupanga losolola m'dzanja lace, lotambasukira pa Yerusalemu. Pamenepo Davide ndi akuru obvala ziguduli anagwa nkhope zao pansi.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 21

Onani 1 Mbiri 21:16 nkhani