1 Mbiri 21:15 BL92

15 Ndipo Mulungu anatuma mthenga ku Yerusalemu kuuononga; ndipo poti auononge, Yehova anapenya, naleka coipaci; nati kwa mthenga wakuononga, Cakwanira, bweza dzanja lako tsopano. Ndi mthenga wa Yehova anaima pa dwale la Orinani Myebusi,

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 21

Onani 1 Mbiri 21:15 nkhani