1 Mbiri 21:3 BL92

3 Nati Yoabu, Yehova aonjezere pa anthu ace monga ali kazana; koma, mbuyanga mfumu, sali onse anyamata akapolo a mbuyanga? nanga afuniranji cinthuci mbuyanga, adzaparamulitsa Israyeli bwanji?

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 21

Onani 1 Mbiri 21:3 nkhani