1 Mbiri 21:2 BL92

2 Ndipo Davide anati kwa Yoabu ndi kwa akuru a anthu, Kawerengeni Israyeli kuyambira ku Beereseba kufikira ku Dani; nimundibwezere mau, kuti ndidziwe ciwerengo cao.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 21

Onani 1 Mbiri 21:2 nkhani