1 Mbiri 22:18 BL92

18 Kodi Yehova Mulungu wanu sali nanu? sanakupumulitsani pambali ponse? pakuti anapereka nzika za m'dziko m'dzanja mwanga, ndi dziko lagonjetsedwa pamaso pa Yehova, ndi pamaso pa anthu ace.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 22

Onani 1 Mbiri 22:18 nkhani