1 Mbiri 22:19 BL92

19 Perekani tsono mtima ndi moyo wanu kufunafuna Yehova Mulungu wanu; ndipo nyamukani ndi kumanga malo opatulika a Yehova Mulungu, kuti abwere nalo likasa la cipangano la Yehova, ndi zipangizo zopatulika za Mulungu, ku nyumba imene idzamangidwira dzina la Yehova.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 22

Onani 1 Mbiri 22:19 nkhani