1 Mbiri 22:9 BL92

9 taona, udzabala mwana, ndiye adzakhala munthu wa phe; ndipo nelidzampumulitsira adani ace onse pozungulirapo, pakuti dzina lace lidzakhala Solomo; ndipo ndidzapatsa Israyeli mtendere ndi bata masiku ace;

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 22

Onani 1 Mbiri 22:9 nkhani