1 Mbiri 27:25 BL92

25 Ndipo woyang'anira cuma ca mfumu ndiye Azimaveti mwana wa Adiyeli, ndi woyang'anira wa cuma ca m'minda, m'mizinda ndi m'miraga, ndi nyumba za nsanja, ndiye Yonatani mwana wa Uziya;

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 27

Onani 1 Mbiri 27:25 nkhani