24 Yoabu mwana wa Zeruya anayamba kuwerenga, koma sanatsiriza; ndi mkwiyo unagwera Israyeli cifukwa ca ici, ndipo ciwerengo cao sicinalembedwa m'buku la mbiri ya mfumu Davide.
Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 27
Onani 1 Mbiri 27:24 nkhani