1 Mbiri 28:18 BL92

18 ndi ca guwa la nsembe lofukizapo la golidi woyengetsa woyesedwa kulemera kwace, ndi cifaniziro ca gareta wa akerubi agolidi akufunyulula mapiko ao ndi kuphimba likasa la cipangano la Yehova.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 28

Onani 1 Mbiri 28:18 nkhani