1 Mbiri 28:8 BL92

8 Ndipo tsopano, pamaso pa Aisrayeli onse, khamu la Yehova, ndi m'makutu a Mulungu wathu, sungani, nimufunefune malamulo onse a Yehova Mulungu wanu, kuti mukhale nalo lanu lanu dziko lokoma ili, ndi kulisiyira ana anu pambuyo panu colowa cao kosalekeza.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 28

Onani 1 Mbiri 28:8 nkhani