22 nadya namwa pamaso pa Mulungu tsiku lomwelo ndi cimwemwe cacikuru. Ndipo analonga ufumu Solomo mwana wa Davide kaciwiri, namdzozera Yehova akhale kalonga, ndi Zadoki akhale wansembe.
Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 29
Onani 1 Mbiri 29:22 nkhani