1 Mbiri 29:22 BL92

22 nadya namwa pamaso pa Mulungu tsiku lomwelo ndi cimwemwe cacikuru. Ndipo analonga ufumu Solomo mwana wa Davide kaciwiri, namdzozera Yehova akhale kalonga, ndi Zadoki akhale wansembe.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 29

Onani 1 Mbiri 29:22 nkhani