1 Mbiri 5:20 BL92

20 Ndipo anathandizidwa polimbana nao; ndi Ahagari anaperekedwa m'dzanja lao, ndi onse anali nao; pakuti anapfuulira kwa Mulungu pomenyana nao, ndipo anapembedzeka nao, popeza anamkhulupirira iye.

Werengani mutu wathunthu 1 Mbiri 5

Onani 1 Mbiri 5:20 nkhani