1 Ndipo Benjamini anabala Bela mwana wace vyoyamba, Asibeli waciwiri, ndi Ahara wacitatu,
2 Noha wacinai, ndi Rafa wacisanu.
3 Ndi Bela anali ndi ana: Adara, ndi Gera, ndi Abihudi,
4 ndi Abisuwa, ndi Namani, ndi Ahowa,
5 ndi Gera, ndi Sefufani, ndi Huramu.
6 Ndi ana a Ehudi ndi awa: ndiwo akuru a nyumba za makolo ao a iwo okhala ku Geba, ndipo anawatenga ndende kumka ku Manahati,