1 Samueli 1:22 BL92

22 Koma Hana sadakwera, cifukwa kuti anati kwa mwamuna wace, Sindidzakwerako kufikira mwanayo ataleka kuyamwa, pamenepo ndidzapita naye kuti aoneke pamaso pa Yehova, ndi kukhalako cikhalire.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 1

Onani 1 Samueli 1:22 nkhani