1 Samueli 1:23 BL92

23 Ndipo Elikana mwamuna wace anati, Cita cimene cikukomera nukhale kufikira utamletsa kuyamwa; komatu Yehova akhazikitse mau ace. Comweco mkaziyo anakhala nayamwitsa mwana wace, kufikira anamletsa kuyamwa.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 1

Onani 1 Samueli 1:23 nkhani