11 Ndipo Yehova anatumiza Yerubaala, ndi Bedani, ndi Yefita, ndi Samueli, napulumutsa inu m'manja mwa adani anu pozungulira ponse, ndipo munakhala mosatekeseka.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 12
Onani 1 Samueli 12:11 nkhani