9 Koma iwowa anaiwala Yehova Mulungu wao, iye nawapereka m'dzanja la Sisera kazembe wa gulu la Hazori, ndi m'dzanja la Afilisti, ndi m'dzanja la mfumu ya Moabu, iwo naponyana nao.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 12
Onani 1 Samueli 12:9 nkhani