15 Ndipo Sauli anati, Anazitenga kwa Aamaleki; pakuti anthu anasunga nkhosa zokometsetsa ndi ng'ombe, kuzipereka nsembe kwa Yehova Mulungu wanu; koma zina tinaziononga konse konse.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 15
Onani 1 Samueli 15:15 nkhani