23 Ndipo anyamata a Sauli analankhula mau awa m'makutu a Davide. Nati Davide, Kodi muciyesera cinthu copepuka kukhala mkamwini wa mfumu, popeza ndiri munthu wosauka, ndi wopeputsidwa.
Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 18
Onani 1 Samueli 18:23 nkhani