1 Samueli 26:6 BL92

6 Pamenepo Davide anayankha nati kwa Ahimeleki Mhiti, ndi Abisai mwana wa Zeruya, mbale wace wa Yoabu, nati, Adzatsikira nane ndani kumisasako kwa Sauli? Nati Abisai, Nditsika nanu ndine.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 26

Onani 1 Samueli 26:6 nkhani