1 Samueli 7:12 BL92

12 Pamenepo Samueli anatenga mwala nauimika pakati pa Mizipa ndi Seni, naucha dzina lace. Ebenezeri, nati, Kufikira pano Yehovaanatithandiza.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 7

Onani 1 Samueli 7:12 nkhani