1 Samueli 9:21 BL92

21 Ndipo Sauli anayankha nati, Sindiri Mbenjamini kodi, wa pfuko laling'ono mwa Israyeli? Ndiponso banja lathu nlocepa pakati pa mabanja onse a pfuko la Benjamini? Potero mulankhula bwanji mau otere ndi ine?

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 9

Onani 1 Samueli 9:21 nkhani