1 Samueli 9:6 BL92

6 Koma ananena naye, Onatu, m'mudzi muno muli munthu wa Mulungu, ndiye munthu anthu amcitira ulemu; zonse azinena zicitika ndithu; tiyeni tipite komweko, kapena adzakhoza kutidziwitsa zimene tirikuyendera.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 9

Onani 1 Samueli 9:6 nkhani