1 Samueli 9:7 BL92

7 Ndipo Sauli ananena ndi mnyamata wace, Koma taona, tikapitako nmtengere ciani munthuyo? popeza mkate udatha m'zotengera zathu, ndiponso tiribe mphatso yakumtengera munthu wa Mulungu, tiri naco ciani?

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 9

Onani 1 Samueli 9:7 nkhani