26 Ndipo khungu langa litaonongeka,Pamenepo wopanda thupi langa, ndidzapenya Mulungu;
27 Amene ndidzampenya ndekha,Ndi maso anga adzamuona, si wina ai.Imso zanga zatha m'kati mwanga.
28 Mukati, Tiyeni timlondole!Popeza cifukwa ca mlandu capezeka mwa ine;
29 Mucite nalo mantha lupanga; Pakuti mkwiyo utenga zolakwa za lupanga,Kuti mudziwe pali ciweruzo.