Yobu 2:10 BL92

10 Koma ananena naye, Ulankhula monga amalankhula akazi opusa. Ha! tidzalandira zokoma kwa Mulungu kodi, osalandiranso zoipa? pa ici conse Yobu sanacimwa ndi milomo yace.

Werengani mutu wathunthu Yobu 2

Onani Yobu 2:10 nkhani