1 Pamenepo Yobu anayankha, nati,
2 Mvetsetsani mau anga;Ndi ici cikhale citonthozo canu.
3 Mundilole, ndinene nanenso; Ndipo nditanena ine, sekani.
4 Kodi ine, kudandaula kwanga, ndidandaulira munthu?Ndipo ndilekerenji kupsa mtima?
5 Ndiyang'anireni, nimusumwe,Gwirani pakamwa panu.
6 Ndikangokumbukila ndibvutika mtima,Ndi thupi langa licita nyau nyau.