19 Agona pansi ali wacuma, koma saikidwa;Potsegula maso ace, wafa cikomo,
20 Zoopsa zimgwera ngati madzi;Nkuntho umtenga usiku.
21 Mphepo ya kum'mawa Imtenga, nacokaiye;Nimkankha acoke m'malo mwace.
22 Pakuti Mulungu adzamponyera zoopsa, osanlieka;Kuthawa akadathawa m'dzanja lace.