Yobu 30:1 BL92

1 Koma tsopano iwo osafikana msinkhu wanga andiseka,Iwo amene atate ao ndikadawapeputsa, osawaika pamodzi ndi agaru olinda nkhosa zanga.

Werengani mutu wathunthu Yobu 30

Onani Yobu 30:1 nkhani