Yobu 7:21 BL92

21 Mulekeranji kukhululukira kulakwa kwanga ndi kundicotsera mphulupulu yanga?Popeza tsopano ndidzagona kupfumbi;Mudzandifunafuna, koma ine palibe.

Werengani mutu wathunthu Yobu 7

Onani Yobu 7:21 nkhani