Macitidwe 13:15 BL92

15 Ndipo m'mene adatha kuwerenga cilamulo ndi aneneri akulu a sunagoge anatuma wina kwa iwo, ndi kunena, Amuna inu, abale, ngati muli nao mau akudandaulira anthu, nenani.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 13

Onani Macitidwe 13:15 nkhani