9 Ndipo masomphenya anaonekera kwa Paulo usiku: Panali munthu wa ku Makedoniya alinkuimirira, namdandaulira kuti, Muolokere ku Makedoniya kuno, mudzatithangate ife.
Werengani mutu wathunthu Macitidwe 16
Onani Macitidwe 16:9 nkhani